Zimene Baibo Imaphunzitsa
Baibo imapeleka mayankho pa mafunso ofunika kwambili mu umoyo. Malangizo ake akhala odalilika kwa zaka mahandiledi. M’cigawo cino, mudzapeza cifukwa cake mungaidalile Baibo, mmene mungapindulile mukamaiŵelenga, komanso mudzaona mmene malangizo ake alili othandiza.—2 Timoteyo 3:16, 17.
Zimene Zilipo
KUYANKHA MAFUNSO A M’BAIBO
Kodi Ndalama N’zimene Zimabweletsa Mavuto Onse?
Zimene anthu ambili amakonda kukamba zakuti “ndalama ndiye muzu wa zoipa zonse” zimangoonetsa kuti samvetsa zimene Baibo imakamba.
KUYANKHA MAFUNSO A M’BAIBO
Kodi Ndalama N’zimene Zimabweletsa Mavuto Onse?
Zimene anthu ambili amakonda kukamba zakuti “ndalama ndiye muzu wa zoipa zonse” zimangoonetsa kuti samvetsa zimene Baibo imakamba.
Phunzilani Baibo
Yambani Kuphunzila Baibo
Landilani maphunzilo a Baibo okambilana na munthu wina kwaulele.
Pemphani kuti wa Mboni adzakucezeleni
Kambilanani nkhani ya m’Baibo na Mboni za Yehova, kapena laŵani maphunzilo a Baibo amene timapeleka.
Zida zophunzilila Baibo
Sankhani zinthu zokuthandizani pophunzila Baibo zimene zingapangitse kuphunzila kwanu kukhala kopindulitsa komanso kokondweletsa.
Kodi Baibo Ingakuthandizeni Bwanji?
Mtendele Komanso Cimwemwe
Baibo yathandiza anthu ambili kupilila mavuto, kucepetsako nkhawa komanso kuthana na mavuto ena ndipo yaŵathandizanso kuona kuti moyo uli na colinga.
Kukhulupilila Mulungu
Cikhulupililo n’camphamvu kwambili ndipo cimathandiza munthu kukhala na mtendele wa mumtima pali pano komanso ciyembekezo codalilika ca m’tsogolo.
Anthu Okwatilana Komanso Mabanja
Anthu okwatilana komanso mabanja amakumana na mavuto ambili. Koma malangizo a m’Baibo angathandize anthu a m’banja kugwilizana komanso kusangalala.
Thandizo kwa Acinyamata
Onani mmene Baibo ingathandizile acinyamata pa mavuto amene amakumana nawo nthawi zambili.
Zocita za Ana
Seŵenzetsani zocita zosangalatsazi, zozikika pa Baibo, pophunzitsa ana makhalidwe auzimu.
Kodi Baibo Imati Ciani?
Kuyankha Mafunso a m’Baibo
Pezani mayankho ocokela m’Baibo okhudza Mulungu, Yesu, banja, mavuto komanso ena ambili.
Kufotokoza Mavesi a m’Baibo
Dziŵani tanthauzo lenileni la mavesi komanso mawu ena odziŵika bwino a m’Baibo.
Mbili Yakale komanso Baibo
Ŵelengani kuti mudziŵe zinacitika kuti Baibo lifikebe mpaka nthawi yathu. Fufuzani umboni woonetsa kuti ni lolondola komanso lodalilika.
Sayansi na Baibo
Kodi Baibo imagwilizana na zimene asayansi amaphunzitsa? Kuyelekezela zimene Baibo imanena na zimene asayansi apeza kungatithandize kupeza yankho la funso limeneli.

