Onani zimene zilipo

Nkhani Zaposacedwa Zimene Zinaonekela pa Tsamba Loyamba

 

Zinsinsi 12 za Banja Lacimwemwe

Kuseŵenzetsa mfundo za m’Baibo zimenezi kungakuthandizeni kukhala na banja lacimwemwe.

Kodi Kuli Mankhwala Othetsela Tsankho?

Kuthetsa tsankho kufunika kuyambila mu mtima na m’maganizo mwathu. Onani mfundo zisanu zimene zingakuthandizeni kuthetsa tsankho.

Pewani Mzimu Wodzikonda Umene Wafala Masiku Ano

Anthu ambili masiku ano amaganiza kuti ayenela kupatsidwa maudindo apadela, komanso kucitilidwa zinthu m’njila yapadela kuposa ena. Onankoni zina mwa mfundo za m’Baibulo zimene zingatithandize kupewa kaganizidwe ka conco.

Kufuna-funa Coonadi

Baibo imapeleka mayankho a zoona pa mafunso ena ofunika kwambili pa umoyo.

Pezani Thandizo pa Nkhawa Zanu

Anthu ambili amavutika na nkhawa. Komabe, pali zambili zimene mungacite kuti mupeze thandizo lofunikila.

Thandizo kwa Acinyamata

Onani mmene Baibo ingathandizile acinyamata pa mavuto amene amakumana nawo nthawi zambili.