Onani zimene zilipo

Kukaona Malo pa Beteli

Tikuitanani kuti mudzaone maofesi athu a nthambi, amene timayacha kuti Beteli. Maofesi ena a nthambi ali na ma miziyamu yakuti munthu akhoza kudzionela yekha zinthu popanda wina kumutsogolela.

Trinidad and Tobago

The Assn of JWs of Trinidad and Tobago

Lower Rapsey St and Laxmi Lane

CUREPE

TRINIDAD AND TOBAGO

+1 868-663-3392

Kuona Malo

Pa Mande mpaka pa Cisanu

8:00hrs mpaka 11:00hrs ndi 13:00hrs mpaka 16:00hrs.

Nthawi yoona malo: Mphindi. 45

Zimene Timacita

Timayang’anila nchito ya Mboni za Yehova m’dziko la Trinidad ndi Tobago, ndiponso ku Guyana.

Tengani kapepala koonetsa malo.