Privacy Settings

To provide you with the best possible experience, we use cookies and similar technologies. Some cookies are necessary to make our website work and cannot be refused. You can accept or decline the use of additional cookies, which we use only to improve your experience. None of this data will ever be sold or used for marketing. To learn more, read the Global Policy on Use of Cookies and Similar Technologies. You can customize your settings at any time by going to Privacy Settings.

Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

Nyimbo 95

“Talawani Ndipo Muone Kuti Yehova Ndi Wabwino”

“Talawani Ndipo Muone Kuti Yehova Ndi Wabwino”

(Salimo 34:8)

1. Kutumikira Mulungu

Kumatisangatsadi.

Ntchito n’njambiri yolalikira

Timaipezera nthawi.

(KOLASI)

M’lungu akuti: ‘Talawani,

Inetu ndi wabwino’

Timapindula tikachita

Zonse zomwe tingathe.

2. Mtumiki wanthawi zonse

M’lungu amamudalitsa.

Amalandira zosowa zake

Amakhala wokhutira.

(KOLASI)

M’lungu akuti: ‘Talawani,

Inetu ndi wabwino’

Timapindula tikachita

Zonse zomwe tingathe.

(Onaninso Maliko 14:8; Luka 21:2; 1 Tim. 1:12; 6:6.)