Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | 1 PETULO 1-2

“Mukhale Oyela”

“Mukhale Oyela”

1:14-16

Tiyenela kukhala oyela, kapena kuti aukhondo, kuti kulambila kwathu kukhale kovomelezeka kwa Yehova. Kodi kumatanthauzanji kukhala woyela . . .

  • mwauzimu?

  • m’makhalidwe?

  • mwakuthupi?