Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 46-47

Thandizo la Cakudya pa Nthawi ya Njala

Thandizo la Cakudya pa Nthawi ya Njala

47:13, 16, 19, 20, 23-25

Masiku ano, anthu m’dzikoli ali na njala yauzimu. (Amosi 8:11) Kupitila mwa Khristu Yesu, Yehova amapeleka cakudya cauzimu ca mwana alilenji.

  • Mabuku ophunzilila Baibo

  • Misonkhano ya mpingo

  • Misonkhano yadela komanso yacigawo

  • Zomvetsela

  • Mavidiyo

  • JW.ORG

  • JW Broadcasting

Kodi nimadzimana zinthu ziti kuti nizidya cakudya cauzimu pa tebulo la Yehova nthawi zonse?