Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | EKSODO 4-5

“Ine Ndidzakhala Nawe Polankhula”

“Ine Ndidzakhala Nawe Polankhula”

4:10-15

Ndi thandizo la Yehova, Mose anagonjetsa mantha ake. Kodi tingaphunzilepo ciani pa zimene Yehova anauza Mose?

  • Tizipewa kusumika maganizo athu pa zinthu zimene timalephela kucita

  • Tiyenela kukhala na cidalilo cakuti Yehova adzatipatsa zonse zofunikila kuti tikwanilitse nchito imene tapatsidwa

  • Cikhulupililo cathu mwa Mulungu cidzatithandiza kuti tisamaope anthu

Kodi Yehova wanithandiza bwanji kupitiliza kulalikila ngakhale panthawi zovuta?