Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Kodi Mumaphunzilapo Kanthu pa Zolakwa Zanu?

Kodi Mumaphunzilapo Kanthu pa Zolakwa Zanu?

[Onetsani vidiyo yakuti Mfundo Zokhudza Buku la 1 Mafumu.]

Adoniya anacitilidwa cifundo pambuyo pokonza ciwembu cakuti akhale mfumu (1 Maf. 1:5, 52, 53; it-2 987 ¶4)

Adoniya sanaphunzilepo kanthu pa colakwa cake, ndipo analangidwa (1 Maf. 2:15-17, 22, 23; it-1 49)

Munthu wanzelu amaphunzilapo kanthu pa zolakwa zake. Koposa pamenepo, amaphunzilapo kanthu pa zolakwa za ena.—1 Akor. 10:11.