Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | 1 TIMOTEYO 1-3

Kalamilani Nchito Yabwino

Kalamilani Nchito Yabwino

3:1, 13

Zimakhala bwino ngati abale ayamba kukalamila ali acicepele. Izi zimawapatsa mwayi wakuti aphunzitsidwe, na kuonetsa kuti ni oyenelela kulandila udindo wokhala mtumiki wothandiza akadzakula. (1 Tim. 3:10) Kodi m’bale angacite ciani kuti akalamile udindo? Angacite zimenezi mwa kukulitsa na kuonetsa makhalidwe otsatilawa:

  • Kudzipeleka pa nchito.—km 7/13 2-3 ¶2

  • Kukonda zinthu zauzimu.—km 7/13 3 ¶3

  • Kudalilika na kukhulupilika.—km 7/13 3 ¶4