Musataye Mtima!
Doris ankadabwa chifukwa chake Mulungu amalola kuti tizivutika. Iye anapeza yankho komwe sankayembekezera.
Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi
NSANJA YA OLONDA
Mafunso Atatu Omwe Anasintha Moyo Wanga
Mphunzitsi anaphunzitsidwa ndi mwana wake wasukulu. Doris Eldred anapeza mayankho ogwira mtima a mafunso ake.
BAIBULO LIMASINTHA ANTHU
Ndinasiya Kupita Kuchipembedzo Chilichonse
Tom ankafunitsitsa kuti azikhulupirira Mulungu koma anakhumudwa ndi zochita komanso miyambo yachabechabe ya chipembedzo. Kodi kuphunzira Baibulo kunamuthandiza bwanji kuti akhale ndi chiyembekezo?
NSANJA YA OLONDA
Ankagwiritsa Ntchito Baibulo Poyankha Funso Lililonse
Isolina Lamela anali sisitere wakatolika koma anakhumudwa ndi zochita za magulu onse awiri. Kenako anakumana ndi a Mboni za Yehova amene anamuthandiza pogwiritsa ntchito Baibulo kuti adziwe chifukwa chake Mulungu anatilenga.
MFUNDO ZOFUNIKA ZA M'BAIBULO
Kodi Mulungu Amavomereza Zipembedzo Zonse?
Anthu amaganiza kuti palibe vuto ngati munthu atalowa m’chipembedzo chilichonse.
BAIBULO LIMASINTHA ANTHU
Ndinkafunitsitsa Kuthana ndi Kupanda Chilungamo
Rafika analowa m’gulu la anthu ofuna kuthana ndi zinthu zopanda chilungamo. Koma anaona kuti m’Baibulo muli lonjezo loti ndi Ufumu wa Mulungu wokha womwe udzabweretse mtendere komanso chilungamo padzikoli.
ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA
Yambani Kuphunzira Baibulo
Phunzirani Baibulo kwaulere, mochita kukambirana ndi mphunzitsi wanu.
BAIBULO LIMASINTHA ANTHU