Zokhudza Kusunga Chinsinsi

Pofuna kukuthandizani kuti musamavutike kuchita zinthu pawebusaiti yathu, timagwiritsa ntchito ma cookies ndiponso njira zina zamakono zofanana ndi zimenezi. Ma cookies ena amathandiza kuti webusaiti yathu izigwira bwino ntchito ndipo sizingatheke kuwakana. Mukhoza kuvomereza kapena kukana ma cookies ena owonjezera, omwe cholinga chake ndi kungokuthandizani kuti musamavutike kuchita zinthu zina pawebusaiti. Sitidzagulitsa kapena kugwiritsa ntchito mauthenga amenewa pofuna kutsatsa malonda. Kuti mudziwe zambiri, werengani Ndondomeko ya Padziko Lonse ya Mmene Timagwiritsira Ntchito ma Cookies ndi Njira Zina Zamakono. Mukhoza kusintha ma settings nthawi ina iliyonse popita pa Zokhudza Kusunga Chinsinsi.

Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

NYIMBO 119

Tikhale Ndi Chikhulupiriro Cholimba

Tikhale Ndi Chikhulupiriro Cholimba

(Aheberi 10:​38, 39)

  1. 1. Kale Mulungu ankalankhula

    Kudzera mwa aneneri.

    Pano kudzera mwa Mwana wake

    Akuti: ‘Lapanitu.’

    (KOLASI)

    Kodi chikhulupiriro

    Chathu ndi cholimba ndithu?

    Chikakhala chenicheni

    M’pamene tingadzapulumuke.

  2. 2. Timamvera lamulo la Yesu

    Loti tizilalikira.

    Tilengezabe molimba mtima,

    Anthu amve uthenga.

    (KOLASI)

    Kodi chikhulupiriro

    Chathu ndi cholimba ndithu?

    Chikakhala chenicheni

    M’pamene tingadzapulumuke.

  3. 3. Talimbitsa chikhulupiriro

    Sitidzabwerera m’mbuyo.

    Tikudziwa kuti M’lungu wathu

    Adzatipulumutsa.

    (KOLASI)

    Kodi chikhulupiriro

    Chathu ndi cholimba ndithu?

    Chikakhala chenicheni

    M’pamene tingadzapulumuke.

 

Tikhale Ndi Chikhulupiriro Cholimba