Phunzirani kwa Anzake a Yehova
Phunzirani zambiri kuchokera kwa anthu otchulidwa m’Baibulo omwe anakhala mabwenzi a Yehova!
Abigayeli
Kodi Abigayeli anathandiza bwanji mnzake kuti apewe zoipa n’kuchita zabwino?
Abele
Kodi mungaphunzire chiyani kwa Abele pa nkhani yolimbitsa chikhulupiriro chanu?
Hananiya, Misayeli, ndi Azariya
Kodi ungamvere Yehova mofanana ndi anzake aja—Hananiya, Misayeli, ndi Azariya?
Pepani, palibe mawu ofanana ndi omwe mwasankha.