Phunzirani kwa Anzake a Yehova

Phunzirani zambiri kuchokera kwa anthu otchulidwa m’Baibulo omwe anakhala mabwenzi a Yehova!

Abigayeli

Kodi Abigayeli anathandiza bwanji mnzake kuti apewe zoipa n’kuchita zabwino?

Abele

Kodi mungaphunzire chiyani kwa Abele pa nkhani yolimbitsa chikhulupiriro chanu?

Hananiya, Misayeli, ndi Azariya

Kodi ungamvere Yehova mofanana ndi anzake aja​—Hananiya, Misayeli, ndi Azariya?

Pepani, palibe mawu ofanana ndi omwe mwasankha.