Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

October 14-​20

1 Petulo 1-2

October 14-​20

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 28

  • Khalani Bwenzi la Yehova​Uzikhala Waukhondo:  (6 min.) Onerani vidiyoyi. Kenako itanani ana omwe munawasankhiratu kuti abwere kutsogolo ndipo muwafunse mafunso otsatirawa: Kodi Mulungu anaika bwanji chilichonse pamalo ake? N’chiyani chimathandiza kuti mvuwu zikhale zaukhondo? N’chifukwa chiyani muyenera kumakonza kuchipinda kwanu?

  • Yehova Amakonda Anthu Aukhondo”: (9 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti, Mulungu Amakonda Anthu Aukhondo.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 55

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 124 ndi Pemphero