Zokhudza Kusunga Chinsinsi

Pofuna kukuthandizani kuti musamavutike kuchita zinthu pawebusaiti yathu, timagwiritsa ntchito ma cookies ndiponso njira zina zamakono zofanana ndi zimenezi. Ma cookies ena amathandiza kuti webusaiti yathu izigwira bwino ntchito ndipo sizingatheke kuwakana. Mukhoza kuvomereza kapena kukana ma cookies ena owonjezera, omwe cholinga chake ndi kungokuthandizani kuti musamavutike kuchita zinthu zina pawebusaiti. Sitidzagulitsa kapena kugwiritsa ntchito mauthenga amenewa pofuna kutsatsa malonda. Kuti mudziwe zambiri, werengani Ndondomeko ya Padziko Lonse ya Mmene Timagwiritsira Ntchito ma Cookies ndi Njira Zina Zamakono. Mukhoza kusintha ma settings nthawi ina iliyonse popita pa Zokhudza Kusunga Chinsinsi.

Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

January 2-8

YESAYA 24-28

January 2-8

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • Yehova Amasamalira Anthu Ake”: (10 min.)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Yes. 26:15—Kodi tingathandize bwanji Yehova pamene ‘akufutukulira kutali malire onse a dzikoli’? (w15 7/15 11 ¶18)

    • Yes. 26:20—Kodi zikuoneka kuti ‘zipinda zamkati’ zikuimira chiyani? (w13 3/15 23 ¶15-16)

    • Kodi ndaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo ziti zimene ndaphunzira pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno zimene ndingazigwiritse ntchito mu utumiki?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Yes. 28:1-13

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Kukonzekera Ulaliki wa Mwezi Uno: (15 min.) Nkhani yokambirana. Pambuyo poonetsa vidiyo ya chitsanzo cha ulaliki iliyonse, kambiranani mfundo zikuluzikulu za m’vidiyoyo. Dziwani izi: Palibe vidiyo ya chitsanzo cha ulaliki wa kapepala kakuti Kodi Mukufuna Kudziwa Choonadi? Choncho pemphani ofalitsa awiri kuti achite chitsanzo cha mmene tingagawirire kapepalaka.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU