Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Zimene Tinganene

Zimene Tinganene

●○ ULENDO WOYAMBA

Funso: Kodi tingapeze kuti malangizo otithandiza kukhala ndi moyo wosangalala?

Lemba: Sl 1:1, 2

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi kukonda ndalama komanso chuma kungathandize munthu kuti akhale ndi moyo wosangalala?

○● ULENDO WOBWEREZA

Funso: Kodi kukonda ndalama komanso chuma kungathandize munthu kuti akhale ndi moyo wosangalala?

Lemba: 1Ti 6:9, 10

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi kuona zinthu moyenera n’kothandiza bwanji?