ONETSANI Buku la m'Baibo Mateyo Maliko Luka Yohane Macitidwe Caputa 1 2 3 4 5 6 7 8 9 10 11 12 13 14 15 16 17 18 19 20 21 22 23 24 25 26 27 28 Macitidwe a Atumwi Macaputala 1 2 3 4 5 6 7 8 9 10 11 12 13 14 15 16 17 18 19 20 21 22 23 24 25 26 27 28 Za m'Bukuli 1 Mawu opita kwa Teofilo (1-5) Kucitila umboni mpaka kumalekezelo a dziko lapansi (6-8) Yesu apita kumwamba (9-11) Ophunzila asonkhana pamodzi mogwilizana (12-14) Matiya asankhidwa kuti alowe m’malo Yudasi (15-26) 2 Anthu alandila mzimu woyela pa Pentekosite (1-13) Nkhani imene Petulo anakamba (14-36) Khamu la anthu licitapo kanthu pa nkhani imene Petulo anakamba (37-41) Anthu 3,000 abatizidwa (41) Akhristu acitila zinthu pamodzi (42-47) 3 Petulo acilitsa munthu wolemala wopemphapempha (1-10) Nkhani imene Petulo anakamba pa Khonde la Zipilala la Solomo (11-26) “Kubwezeletsa zinthu zonse” (21) Mneneli ngati Mose (22) 4 Petulo ndi Yohane amangidwa (1-4) Amuna okhulupilila akwana 5,000 (4) Aweluzidwa pamaso pa Khoti Yaikulu ya Ayuda (5-22) “Ife sitingaleke kulankhula” (20) Apemphela kuti akhale olimba mtima (23-31) Ophunzila agawana zinthu (32-37) 5 Hananiya ndi Safira (1-11) Atumwi acita zizindikilo zambili (12-16) Amangidwa kenako amasulidwa (17-21a) Apelekedwanso ku Khoti Yaikulu ya Ayuda (21b-32) ‘Kumvela Mulungu osati anthu’ (29) Ulangizi wa Gamaliyeli (33-40) Kulalikila kunyumba ndi nyumba (41, 42) 6 Amuna 7 asankhidwa kuti atumikile (1-7) Sitefano aimbidwa mlandu wonyoza Mulungu (8-15) 7 Sitefano alankhula pamaso pa Khoti Yaikulu ya Ayuda (1-53) Nthawi ya makolo akale (2-16) Utsogoleli wa Mose; Aisiraeli alambila mafano (17-43) Mulungu sakhala mu akacisi opangidwa ndi anthu (44-50) Sitefano aponyedwa miyala (54-60) 8 Saulo azunza ophunzila (1-3) Utumiki wa Filipo ubala zipatso ku Samariya (4-13) Petulo ndi Yohane atumidwa ku Samariya (14-17) Simoni afuna kugula mzimu woyela (18-25) Nduna ya ku Itiyopiya (26-40) 9 Saulo ali pa ulendo wopita ku Damasiko (1-9) Hananiya atumizidwa kuti akathandize Saulo (10-19a) Saulo alalikila za Yesu ku Damasiko (19b-25) Saulo apita ku Yerusalemu (26-31) Petulo acilitsa Eneya (32-35) Dorika wowolowa manja aukitsidwa (36-43) 10 Masomphenya a Koneliyo (1-8) Petulo aona masomphenya a nyama zoyeletsedwa (9-16) Petulo apita kunyumba kwa Koneliyo (17-33) Petulo alengeza uthenga wabwino kwa anthu a mitundu ina (34-43) “Mulungu alibe tsankho” (34, 35) Anthu a mitundu ina alandila mzimu woyela ndipo abatizidwa (44-48) 11 Petulo apeleka lipoti kwa atumwi (1-18) Baranaba ndi Saulo ku Antiokeya wa ku Siriya (19-26) Ophunzila ayamba kuchedwa Akhristu (26) Agabo alosela za njala (27-30) 12 Yakobo aphedwa; Petulo aponyedwa m’ndende (1-5) Petulo amasulidwa mozizwitsa (6-19) Herode akanthidwa ndi mngelo (20-25) 13 Baranaba ndi Saulo atumizidwa ngati amishonale (1-3) Utumiki wa ku Kupuro (4-12) Zimene Paulo anakamba ku Antiokeya wa ku Pisidiya (13-41) Ulosi wakuti ayambe kulalikila anthu a mitundu ina (42-52) 14 Okhulupilila awonjezeka ku Ikoniyo ndipo ayamba kutsutsidwa (1-7) Aonedwa monga milungu ku Lusitara (8-18) Paulo apulumuka atamuponya miyala (19, 20) Kulimbikitsa mipingo (21-23) Abwelela ku Antiokeya wa ku Siriya (24-28) 15 Atsutsana pa nkhani ya mdulidwe ku Antiokeya (1, 2) Apeleka nkhaniyi ku Yerusalemu (3-5) Akulu ndi atumwi akumana pamodzi (6-21) Kalata yocokela ku bungwe lolamulila (22-29) Pewani magazi (28, 29) Mipingo ilimbikitsidwa ndi kalata (30-35) Paulo ndi Baranaba apatukana (36-41) 16 Paulo asankha Timoteyo (1-5) Munthu wa ku Makedoniya aonekela m’masomphenya (6-10) Lidiya akhala Mkhristu ku Filipi (11-15) Paulo ndi Sila aponyedwa m’ndende (16-24) Woyang’anila ndende ndi a m’banja lake abatizika (25-34) Paulo apempha akuluakulu a zamalamulo kuti apepese (35-40) 17 Paulo ndi Sila ku Tesalonika (1-9) Paulo ndi Sila ku Bereya (10-15) Paulo ku Atene (16-22a) Zimene Paulo ananena ku bwalo la Areopagi (22b-34) 18 Utumiki wa Paulo ku Korinto (1-17) Abwelela ku Antiokeya wa ku Siriya (18-22) Paulo acoka n’kupita ku Galatiya ndi ku Filigiya (23) Apolo wolankhula mwaluso athandizidwa (24-28) 19 Paulo ku Efeso; ena abatizika kaciwili (1-7) Nchito yophunzitsa ya Paulo (8-10) Apeza cipambano ngakhale kuti ena anali kukhulupilila zamizimu (11-20) Cipolowe ku Efeso (21-41) 20 Paulo ku Makedoniya ndi ku Girisi (1-6) Utiko aukitsidwa ku Torowa (7-12) Acoka ku Torowa n’kupita ku Mileto (13-16) Paulo akumana ndi akulu a ku Efeso (17-38) Aphunzitsa kunyumba ndi nyumba (20) “Kupatsa kumabweletsa cimwemwe cacikulu” (35) 21 Ulendo wa ku Yerusalemu (1-14) Afika ku Yerusalemu (15-19) Paulo atsatila malangizo a akulu (20-26) Cipolowe m’kacisi; Paulo agwidwa (27-36) Paulo aloledwa kuti alankhule ndi khamu la anthu (37-40) 22 Mawu a Paulo odziteteza pamaso pa khamu la anthu (1-21) Paulo agwilitsa nchito unzika wake wokhala m’Roma (22-29) Khoti Yaikulu ya Ayuda isonkhana (30) 23 Paulo alankhula pamaso pa Khoti Yaikulu ya Ayuda (1-10) Ambuye alimbikitsa Paulo (11) Ciwembu cofuna kupha Paulo (12-22) Paulo atumizidwa ku Kaisareya (23-35) 24 Paulo aimbidwa milandu (1-9) Paulo adziteteza pamaso pa Felike (10-21) Mlandu wa Paulo uyedzekedwa kwa zaka ziwili (22-27) 25 Paulo afotokoza mlandu wake pamaso pa Fesito (1-12) “Ndikucita apilo kuti ndikaonekele kwa Kaisara!” (11) Fesito afunsila nzelu kwa Mfumu Agiripa (13-22) Paulo aonekela pamaso pa Agiripa (23-27) 26 Paulo adziteteza pamaso pa Agiripa (1-11) Paulo afotokoza mmene anakhalila Mkhristu (12-23) Zimene Fesito ndi Agiripa anacita (24-32) 27 Paulo ayamba ulendo wa panyanja wopita ku Roma (1-12) Namondwe awomba ngalawa (13-38) Ngalawa ipasuka (39-44) 28 Gombe la ku Melita (1-6) Atate ake Papuliyo acilitsidwa (7-10) Ulendo wa ku Roma (11-16) Paulo alankhula ndi Ayuda ku Roma (17-29) Paulo alalikila molimba mtima kwa zaka ziwili (30, 31) Yakumbuyo Yotsatila Pulintani Gaŵilani Gaŵilani Macitidwe—za m’Bukuli BAIBO YA CIMASULILO CA DZIKO LATSOPANO Macitidwe—za m’Bukuli Cinyanja Macitidwe—za m’Bukuli https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/1001061100/univ/wpub/1001061100_univ_sqr_xl.jpg nwt Machitidwe