NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA) July 2025

M’magaziniyi muli nkhani zophunzira kuyambira September 15–October 12, 2025.

NKHANI YOPHUNZIRA 28

N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kupempha Malangizo?

Idzaphunziridwa mlungu woyambira September 15-21, 2025.

NKHANI YOPHUNZIRA 29

Zimene Tingachite Kuti Tizipereka Malangizo Abwino

Idzaphunziridwa mlungu woyambira September 22-28, 2025.

NKHANI YOPHUNZIRA 30

Kodi Mfundo Zoyambirira za M’Baibulo Zingakuthandizenibe Masiku Ano?

Idzaphunziridwa mlungu woyambira September 29–October 5, 2025.

NKHANI YOPHUNZIRA 31

Kodi ‘Mwaphunzira Chinsinsi’ Chokhala Wokhutira?

Idzaphunziridwa mlungu woyambira October 6-12, 2025.

MBIRI YA MOYO WANGA

“Yehova Ndiye Mwini Nkhondo”

Pa zaka 40 zapitazi, M’bale Philip Brumley wakhala ndi mwayi wogwira ntchito ndi abale m’maofesi a nthambi padziko lonse pa nkhani zamalamulo komanso kuonekera m’makhoti osiyanasiyana ndiponso pamaso pa akuluakulu a boma. Iye akuti zimenezi zamuthandiza kutsimikizira kuti Yehova ndi amene amapereka mphamvu komanso luso kwa atumiki ake kuti apambane.

Kodi Mukudziwa?

Kodi ansembe a pakachisi ankatani ndi magazi a nyama zomwe zaperekedwa nsembe paguwa?

MFUNDO ZOTHANDIZA POPHUNZIRA

Muziuza Ena Zimene Mwaphunzira

Kuuza ena zimene taphunzira kungatithandize kuti tizikumbukira komanso kumvetsa bwino zinthu.