CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MALIRO 1-5

Mtima Wodikira Umatithandiza Kuti Tipirire

Mtima Wodikira Umatithandiza Kuti Tipirire

Kodi n’chiyani chinathandiza kuti Yeremiya apirire ngakhale kuti anakumana ndi mavuto aakulu?

3:20, 21, 24, 26, 27

  • Iye ankakhulupirira ndi mtima wonse kuti Yehova ‘adzaweramira’ anthu ake omwe analapa n’kuwapulumutsa m’mavuto awo

  • Iye anaphunzira ‘kunyamula goli lake ali mnyamata.’ Munthu akamapirira mayesero ali wamng’ono zimamuthandiza kuti adzathe kupirira mavuto omwe angadzakumane nawo m’tsogolo

Yeremiya akupemphera ataona kuti anthu a ku Yerusalemu atengedwa kupita kuukapolo

Kodi ndingakonzekere bwanji mavuto amene ndingakumane nawo m’tsogolo?

 

Kodi ndingasonyeze bwanji kuti ndili ndi mtima wodikira?